Salmos 123

NYA

1 Ndikweza maso anga kwa Inu,

2 Taonani, monga momwe maso a akapolo amayangʼana mʼdzanja la mbuye wawo,

3 Mutichitire chifundo, Inu Yehova mutichitire chifundo,

4 Ife tapirira mnyozo wambiri kuchokera kwa anthu odzikuza,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado