1 Ndikweza maso anga kwa Inu,
2 Taonani, monga momwe maso a akapolo amayangʼana mʼdzanja la mbuye wawo,
3 Mutichitire chifundo, Inu Yehova mutichitire chifundo,
4 Ife tapirira mnyozo wambiri kuchokera kwa anthu odzikuza,
NYA
1 Ndikweza maso anga kwa Inu,
2 Taonani, monga momwe maso a akapolo amayangʼana mʼdzanja la mbuye wawo,
3 Mutichitire chifundo, Inu Yehova mutichitire chifundo,
4 Ife tapirira mnyozo wambiri kuchokera kwa anthu odzikuza,