Salmos 121

NYA

1 Ndikweza maso anga ku mapiri;

2 Thandizo langa limachokera kwa Yehova,

3 Sadzalola kuti phazi lako literereke;

4 Taonani, Iye amene amasunga Israeli

5 Yehova ndiye amene amakusunga;

6 Dzuwa silidzakupweteka nthawi ya masana,

7 Yehova adzakuteteza ku zoyipa zonse;

8 Yehova adzayangʼanira kutuluka kwako ndi kulowa kwako;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado