1 Ndikweza maso anga ku mapiri;
2 Thandizo langa limachokera kwa Yehova,
3 Sadzalola kuti phazi lako literereke;
4 Taonani, Iye amene amasunga Israeli
5 Yehova ndiye amene amakusunga;
6 Dzuwa silidzakupweteka nthawi ya masana,
7 Yehova adzakuteteza ku zoyipa zonse;
8 Yehova adzayangʼanira kutuluka kwako ndi kulowa kwako;