Salmos 114

NYA

1 Pamene Israeli anatuluka mu Igupto,

2 Yuda anasanduka malo opatulika a Mulungu,

3 Nyanja inaona ndi kuthawa,

4 mapiri analumphalumpha ngati nkhosa zazimuna,

5 Nʼchifukwa chiyani iwe unathawa?

6 inu mapiri, munalumphalumphiranji ngati nkhosa zazimuna,

7 Njenjemera pamaso pa Ambuye iwe dziko lapansi,

8 amene anasandutsa thanthwe kukhala chitsime,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado