1 Pamene Israeli anatuluka mu Igupto,
2 Yuda anasanduka malo opatulika a Mulungu,
3 Nyanja inaona ndi kuthawa,
4 mapiri analumphalumpha ngati nkhosa zazimuna,
5 Nʼchifukwa chiyani iwe unathawa?
6 inu mapiri, munalumphalumphiranji ngati nkhosa zazimuna,
7 Njenjemera pamaso pa Ambuye iwe dziko lapansi,
8 amene anasandutsa thanthwe kukhala chitsime,