1 Kwa ife ayi Yehova, kwa ife ayi
2 Chifukwa chiyani anthu a mitundu ina akunena kuti,
3 Mulungu wathu ali kumwamba;
4 Koma mafano awo ndi siliva ndi golide,
5 Pakamwa ali napo koma sayankhula,
6 makutu ali nawo koma samva,
7 manja ali nawo koma akakhudza samva kanthu;
8 Anthu amene amapanga mafanowo adzafanana nawo,
9 Inu Aisraeli, dalirani Yehova;
10 Iwe nyumba ya Aaroni, dalira Yehova;
11 Inu amene mumaopa Iye, dalirani Yehova;
12 Yehova watikumbukira ndipo adzatidalitsa:
13 adzadalitsa iwo amene amaopa Yehova;
14 Yehova akuwonjezereni madalitso;
15 Mudalitsidwe ndi Yehova,
16 Kumwamba ndi kwa Yehova,
17 Si anthu akufa amene amatamanda Yehova,
18 ndi ife amene timatamanda Yehova,