Salmos 115

NYA

1 Kwa ife ayi Yehova, kwa ife ayi

2 Chifukwa chiyani anthu a mitundu ina akunena kuti,

3 Mulungu wathu ali kumwamba;

4 Koma mafano awo ndi siliva ndi golide,

5 Pakamwa ali napo koma sayankhula,

6 makutu ali nawo koma samva,

7 manja ali nawo koma akakhudza samva kanthu;

8 Anthu amene amapanga mafanowo adzafanana nawo,

9 Inu Aisraeli, dalirani Yehova;

10 Iwe nyumba ya Aaroni, dalira Yehova;

11 Inu amene mumaopa Iye, dalirani Yehova;

12 Yehova watikumbukira ndipo adzatidalitsa:

13 adzadalitsa iwo amene amaopa Yehova;

14 Yehova akuwonjezereni madalitso;

15 Mudalitsidwe ndi Yehova,

16 Kumwamba ndi kwa Yehova,

17 Si anthu akufa amene amatamanda Yehova,

18 ndi ife amene timatamanda Yehova,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado