Salmos 113

NYA

1 Tamandani Yehova.

2 Yehova atamandidwe,

3 Kuyambira ku matulukiro a dzuwa mpaka ku malowero ake,

4 Yehova wakwezeka pa anthu a mitundu yonse,

5 Ndani wofanana ndi Yehova Mulungu wathu,

6 amene amawerama pansi kuyangʼana

7 Iye amakweza munthu wosauka kuchoka pa fumbi

8 amawakhazika pamodzi ndi mafumu,

9 Amakhazikitsa mayi wosabereka mʼnyumba yake

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado