1 Tamandani Yehova.
2 Yehova atamandidwe,
3 Kuyambira ku matulukiro a dzuwa mpaka ku malowero ake,
4 Yehova wakwezeka pa anthu a mitundu yonse,
5 Ndani wofanana ndi Yehova Mulungu wathu,
6 amene amawerama pansi kuyangʼana
7 Iye amakweza munthu wosauka kuchoka pa fumbi
8 amawakhazika pamodzi ndi mafumu,
9 Amakhazikitsa mayi wosabereka mʼnyumba yake