Salmos 112

NYA

1 Tamandani Yehova.

2 Ana ake adzakhala amphamvu mʼdziko;

3 Kulemera ndi chuma zili mʼnyumba yake,

4 Ngakhale mu mdima kuwala kumatulukira olungama mtima;

5 Zinthu zabwino zidzabwera kwa iye amene amapereka mowolowamanja ndi wokongoletsa mwaufulu,

6 Ndithu sadzagwedezeka;

7 Saopa akamva zoyipa zimene zachitika;

8 Mtima wake ndi wotetezedwa, sadzakhala ndi mantha;

9 Wopereka mphatso zake mowolowamanja kwa osauka,

10 Munthu woyipa adzaona zimenezi ndipo adzapsa mtima;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado