Salmos 111

NYA

1 Tamandani Yehova.

2 Ntchito za Yehova nʼzazikulu;

3 Zochita zake ndi za ulemerero ndi zaufumu,

4 Iye wachititsa kuti zodabwitsa zake zikumbukirike;

5 Amapereka chakudya kwa amene amamuopa Iye;

6 Waonetsa anthu ake mphamvu ya ntchito zake,

7 Ntchito za manja ake ndi zokhulupirika ndi zolungama;

8 Malamulo ndi okhazikika ku nthawi za nthawi,

9 Iyeyo amawombola anthu ake;

10 Kuopa Yehova ndicho chiyambi cha nzeru;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado