1 Tamandani Yehova.
2 Ntchito za Yehova nʼzazikulu;
3 Zochita zake ndi za ulemerero ndi zaufumu,
4 Iye wachititsa kuti zodabwitsa zake zikumbukirike;
5 Amapereka chakudya kwa amene amamuopa Iye;
6 Waonetsa anthu ake mphamvu ya ntchito zake,
7 Ntchito za manja ake ndi zokhulupirika ndi zolungama;
8 Malamulo ndi okhazikika ku nthawi za nthawi,
9 Iyeyo amawombola anthu ake;
10 Kuopa Yehova ndicho chiyambi cha nzeru;