1 Mtima wanga ndi wokhazikika, Inu Mulungu;
2 Dzukani, zeze ndi pangwe!
3 Ndidzakutamandani Yehova, pakati pa anthu a mitundu ina;
4 Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu, kutalika kwake kuposa kumwamba;
5 Kwezekani Inu Mulungu, kuposa mayiko akumwamba,
6 Tipulumutseni ndi kutithandiza ndi dzanja lanu lamanja
7 Mulungu wayankhula kuchokera ku malo ake opatulika:
8 Giliyadi ndi wanga, Manase ndi wanganso;
9 Mowabu ndi mbale yanga yosambiramo
10 Ndani adzandifikitsa ku mzinda wotetezedwa?
11 Kodi sindinu Mulungu, Inu amene mwatikana
12 Tithandizeni ife kulimbana ndi mdani,
13 Chifukwa cha Mulungu wathu, ife tidzapeza chipambano,