Salmos 109

NYA

1 Mulungu amene ndimakutamandani,

2 pakuti anthu oyipa ndi achinyengo

3 Andizungulira ndi mawu audani,

4 Mʼmalo mwa chikondi changa amandineneza,

5 Iwo amandibwezera zoyipa mʼmalo mwa zabwino,

6 Sankhani munthu woyipa kuti amutsutse iye;

7 Pamene aweruzidwa, apezeke kuti ndi wolakwa,

8 Masiku ake akhale owerengeka;

9 Ana ake akhale amasiye

10 Ana ake akhale oyendayenda ndi opemphapempha;

11 Wokongoza alande zonse zimene ali nazo;

12 Pasapezeke ndi mmodzi yemwe womukomera mtima

13 Zidzukulu zake zithe nʼkufa,

14 Mphulupulu za makolo ake zikumbukiridwe pamaso pa Yehova;

15 Machimo awo akhale pamaso pa Yehova nthawi zonse,

16 Pakuti iye sanaganizirepo zochita chifundo,

17 Anakonda kutemberera,

18 Anavala kutemberera ngati chovala;

19 Matemberero akhale ngati chofunda chodzikutira nacho,

20 Awa akhale malipiro ochokera kwa Yehova pa onditsutsa anga,

21 Koma Inu Ambuye Wamphamvuzonse,

22 Pakuti ndine wosauka ndi wosowa,

23 Ndikuzimirira ngati mthunzi wa kumadzulo,

24 Mawondo anga afowoka chifukwa cha kusala zakudya,

25 Ndine chinthu chotonzedwa kwa otsutsana nane;

26 Thandizeni Inu Yehova Mulungu wanga;

27 Adaniwo adziwe kuti limeneli ndi dzanja lanu,

28 Angathe kutemberera, koma Inu mudzadalitsa;

29 Onditsutsa adzavekedwa mnyozo,

30 Ndi pakamwa panga ndidzathokoza Yehova kwambiri;

31 Popeza Iye amayima ku dzanja lamanja la munthu wosowayo,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado