1 Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino;
2 Owomboledwa a Yehova anene zimenezi
3 iwo amene anawasonkhanitsa kuchokera ku mayiko,
4 Ena anayendayenda mʼchipululu mopanda kanthu,
5 Iwo anamva njala ndi ludzu,
6 Pamenepo analirira Yehova mʼmavuto awo
7 Iye anawatsogolera mʼnjira yowongoka
8 Ayamike Yehova chifukwa cha chikondi chake chosatha
9 pakuti Iye wapha ludzu la munthu womva ludzu
10 Ena anakhala mu mdima ndi mʼchisoni chachikulu,
11 pakuti iwowo anawukira mawu a Mulungu
12 Kotero Iye anawapereka kuti agwire ntchito yakalavulagaga;
13 Pamenepo analirira Yehova mʼmasautso awo
14 Yehova anawatulutsa mu mdima ndi mʼchisoni chachikulu
15 Ayamike Yehova chifukwa cha chikondi chake chosatha
16 pakuti Iye amathyola zipata zamkuwa
17 Ena anakhala zitsiru chifukwa cha njira zawo zowukira,
18 Iwo ananyansidwa ndi chakudya chilichonse
19 Pamenepo analirira Yehova mʼmasautso awo
20 Iye anatumiza mawu ake ndi kuwachiritsa;
21 Ayamike Yehova chifukwa cha chikondi chake chosatha
22 Apereke nsembe yachiyamiko
23 Ena anayenda pa nyanja mʼsitima zapamadzi;
24 Anaona ntchito za Yehova,
25 Pakuti Iye anayankhula ndi kuwutsa mphepo yamkuntho
26 Sitima za pamadzizo zinatukulidwa mmwamba ndi kutsikira pansi pakuya;
27 Anachita chizungulire ndi kudzandira ngati anthu oledzera;
28 Pamenepo analirira Yehova mʼmasautso awo
29 Yehova analetsa namondwe,
30 Anali osangalala pamene kunakhala bata,
31 Ayamike Yehova chifukwa cha chikondi chake chosatha
32 Akuze Iye mu msonkhano wa anthu
33 Iye anasandutsa mitsinje kukhala chipululu,
34 ndiponso nthaka yachonde kukhala nthaka yamchere,
35 Anasandutsa chipululu kukhala mayiwe a madzi
36 kumeneko Iye anabweretsa anthu anjala kuti azikhalako,
37 Anafesa mbewu mʼminda ndi kudzala mipesa
38 Yehova anawadalitsa, ndipo chiwerengero chawo chinachuluka kwambiri,
39 Kenaka chiwerengero chawo chinachepa ndipo iwo anatsitsidwa
40 Iye amene amakhuthulira mʼnyozo pa olemekezeka
41 Koma Iyeyo anakweza anthu osowa kuchoka ku masautso awo
42 Anthu olungama mtima amaona ndi kusangalala,
43 Aliyense wanzeru asamalitse zinthu zimenezi