Salmos 107

NYA

1 Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino;

2 Owomboledwa a Yehova anene zimenezi

3 iwo amene anawasonkhanitsa kuchokera ku mayiko,

4 Ena anayendayenda mʼchipululu mopanda kanthu,

5 Iwo anamva njala ndi ludzu,

6 Pamenepo analirira Yehova mʼmavuto awo

7 Iye anawatsogolera mʼnjira yowongoka

8 Ayamike Yehova chifukwa cha chikondi chake chosatha

9 pakuti Iye wapha ludzu la munthu womva ludzu

10 Ena anakhala mu mdima ndi mʼchisoni chachikulu,

11 pakuti iwowo anawukira mawu a Mulungu

12 Kotero Iye anawapereka kuti agwire ntchito yakalavulagaga;

13 Pamenepo analirira Yehova mʼmasautso awo

14 Yehova anawatulutsa mu mdima ndi mʼchisoni chachikulu

15 Ayamike Yehova chifukwa cha chikondi chake chosatha

16 pakuti Iye amathyola zipata zamkuwa

17 Ena anakhala zitsiru chifukwa cha njira zawo zowukira,

18 Iwo ananyansidwa ndi chakudya chilichonse

19 Pamenepo analirira Yehova mʼmasautso awo

20 Iye anatumiza mawu ake ndi kuwachiritsa;

21 Ayamike Yehova chifukwa cha chikondi chake chosatha

22 Apereke nsembe yachiyamiko

23 Ena anayenda pa nyanja mʼsitima zapamadzi;

24 Anaona ntchito za Yehova,

25 Pakuti Iye anayankhula ndi kuwutsa mphepo yamkuntho

26 Sitima za pamadzizo zinatukulidwa mmwamba ndi kutsikira pansi pakuya;

27 Anachita chizungulire ndi kudzandira ngati anthu oledzera;

28 Pamenepo analirira Yehova mʼmasautso awo

29 Yehova analetsa namondwe,

30 Anali osangalala pamene kunakhala bata,

31 Ayamike Yehova chifukwa cha chikondi chake chosatha

32 Akuze Iye mu msonkhano wa anthu

33 Iye anasandutsa mitsinje kukhala chipululu,

34 ndiponso nthaka yachonde kukhala nthaka yamchere,

35 Anasandutsa chipululu kukhala mayiwe a madzi

36 kumeneko Iye anabweretsa anthu anjala kuti azikhalako,

37 Anafesa mbewu mʼminda ndi kudzala mipesa

38 Yehova anawadalitsa, ndipo chiwerengero chawo chinachuluka kwambiri,

39 Kenaka chiwerengero chawo chinachepa ndipo iwo anatsitsidwa

40 Iye amene amakhuthulira mʼnyozo pa olemekezeka

41 Koma Iyeyo anakweza anthu osowa kuchoka ku masautso awo

42 Anthu olungama mtima amaona ndi kusangalala,

43 Aliyense wanzeru asamalitse zinthu zimenezi

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado