Salmos 106

NYA

1 Tamandani Yehova.

2 Ndani angathe kufotokoza za ntchito zamphamvu za Yehova

3 Odala ndi amene amasunga chilungamo,

4 Mundikumbukire Yehova, pamene mukuonetsa kukoma mtima kwanu kwa anthu anu,

5 kuti ndidzasangalale ndi chuma cha anthu anu osankhika,

6 Ife tachimwa monga momwe anachitira makolo athu;

7 Pamene makolo athu anali mu Igupto,

8 Komabe Iye anawapulumutsa chifukwa cha dzina lake,

9 Anadzudzula Nyanja Yofiira, ndipo inawuma;

10 Anawapulumutsa mʼdzanja la amaliwongo;

11 Madzi anamiza adani awo,

12 Kenaka iwo anakhulupirira malonjezo ake

13 Koma posachedwa anayiwala zimene Iye anachita,

14 Mʼchipululu, anadzipereka ku zilakolako zawo;

15 Choncho Iye anawapatsa chimene anapempha,

16 Mʼmisasa, anachitira nsanje Mose ndi Aaroni,

17 Nthaka inatsekuka ndipo inameza Datani;

18 Moto unayaka pakati pa otsatira awo;

19 Iwo anapanga mwana wangʼombe pa Horebu

20 Anasinthanitsa ulemerero wawo

21 Anayiwala Mulungu amene anawapulumutsa,

22 zozizwitsa mʼdziko la Hamu

23 Choncho Iye anawawuza kuti adzawawononga,

24 Motero iwo ananyoza dziko lokoma;

25 Anangʼungʼudza mʼmatenti mwawo

26 Kotero Iye analumbira atakweza dzanja lake,

27 kuchititsa kuti zidzukulu zawo zifere pakati pa anthu a mitundu ina

28 Iwo anayamba kupembedza Baala-Peori

29 anaputa mkwiyo wa Yehova pa machitidwe awo oyipa,

30 Koma Finehasi anayimirira ndi kulowererapo,

31 Chimenechi ndicho chinayesedwa chilungamo chake,

32 Pa madzi a ku Meriba iwo anakwiyitsa Yehova

33 pakuti iwowo anawukira mzimu wa Mulungu,

34 Aisraeliwo sanawononge mitundu ya anthu

35 Koma anasakanizana ndi anthu a mitundu inayo

36 Ndipo anapembedza mafano awo,

37 Anapereka nsembe ana awo aamuna

38 Anakhetsa magazi a anthu osalakwa,

39 Iwo anadzidetsa okha ndi zimene anachita;

40 Tsono Yehova anakwiya ndi anthu ake

41 Iye anawapereka kwa anthu a mitundu ina,

42 Adani awo anawazunza

43 Iye ankawapulumutsa nthawi zambiri,

44 Koma Iye anaona kuzunzika kwawo

45 Chifukwa cha iwo Iye anakumbukira pangano lake

46 Iye anachititsa kuti amene anawagwira iwo ukapolo

47 Tipulumutseni Inu Yehova Mulungu wathu,

48 Atamandike Yehova, Mulungu wa Israeli,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado