1 Tamandani Yehova.
2 Ndani angathe kufotokoza za ntchito zamphamvu za Yehova
3 Odala ndi amene amasunga chilungamo,
4 Mundikumbukire Yehova, pamene mukuonetsa kukoma mtima kwanu kwa anthu anu,
5 kuti ndidzasangalale ndi chuma cha anthu anu osankhika,
6 Ife tachimwa monga momwe anachitira makolo athu;
7 Pamene makolo athu anali mu Igupto,
8 Komabe Iye anawapulumutsa chifukwa cha dzina lake,
9 Anadzudzula Nyanja Yofiira, ndipo inawuma;
10 Anawapulumutsa mʼdzanja la amaliwongo;
11 Madzi anamiza adani awo,
12 Kenaka iwo anakhulupirira malonjezo ake
13 Koma posachedwa anayiwala zimene Iye anachita,
14 Mʼchipululu, anadzipereka ku zilakolako zawo;
15 Choncho Iye anawapatsa chimene anapempha,
16 Mʼmisasa, anachitira nsanje Mose ndi Aaroni,
17 Nthaka inatsekuka ndipo inameza Datani;
18 Moto unayaka pakati pa otsatira awo;
19 Iwo anapanga mwana wangʼombe pa Horebu
20 Anasinthanitsa ulemerero wawo
21 Anayiwala Mulungu amene anawapulumutsa,
22 zozizwitsa mʼdziko la Hamu
23 Choncho Iye anawawuza kuti adzawawononga,
24 Motero iwo ananyoza dziko lokoma;
25 Anangʼungʼudza mʼmatenti mwawo
26 Kotero Iye analumbira atakweza dzanja lake,
27 kuchititsa kuti zidzukulu zawo zifere pakati pa anthu a mitundu ina
28 Iwo anayamba kupembedza Baala-Peori
29 anaputa mkwiyo wa Yehova pa machitidwe awo oyipa,
30 Koma Finehasi anayimirira ndi kulowererapo,
31 Chimenechi ndicho chinayesedwa chilungamo chake,
32 Pa madzi a ku Meriba iwo anakwiyitsa Yehova
33 pakuti iwowo anawukira mzimu wa Mulungu,
34 Aisraeliwo sanawononge mitundu ya anthu
35 Koma anasakanizana ndi anthu a mitundu inayo
36 Ndipo anapembedza mafano awo,
37 Anapereka nsembe ana awo aamuna
38 Anakhetsa magazi a anthu osalakwa,
39 Iwo anadzidetsa okha ndi zimene anachita;
40 Tsono Yehova anakwiya ndi anthu ake
41 Iye anawapereka kwa anthu a mitundu ina,
42 Adani awo anawazunza
43 Iye ankawapulumutsa nthawi zambiri,
44 Koma Iye anaona kuzunzika kwawo
45 Chifukwa cha iwo Iye anakumbukira pangano lake
46 Iye anachititsa kuti amene anawagwira iwo ukapolo
47 Tipulumutseni Inu Yehova Mulungu wathu,
48 Atamandike Yehova, Mulungu wa Israeli,