Sofonias 2

NYA

1 Sonkhanani pamodzi, sonkhanani pamodzi,

2 isanafike nthawi yachiweruzo,

3 Funafunani Yehova, inu nonse odzichepetsa a mʼdziko,

4 Gaza adzasiyidwa

5 Tsoka inu okhala mʼmbali mwa nyanja,

6 Dziko la mʼmbali mwa nyanja, kumene kumakhala Akereti,

7 Malowa adzakhala a anthu otsala a nyumba ya Yuda;

8 “Ndamva kunyoza kwa Mowabu

9 Choncho, pali Ine Wamoyo,”

10 Ichi ndi chimene adzalandire chifukwa cha kunyada kwawo,

11 Yehova adzawachititsa mantha kwambiri

12 “Inunso anthu a ku Kusi,

13 Yehova adzatambasulira dzanja lake kumpoto

14 Nkhosa ndi ngʼombe zidzagona pansi kumeneko,

15 Umenewu ndiye mzinda wosasamala

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado