1 Sonkhanani pamodzi, sonkhanani pamodzi,
2 isanafike nthawi yachiweruzo,
3 Funafunani Yehova, inu nonse odzichepetsa a mʼdziko,
4 Gaza adzasiyidwa
5 Tsoka inu okhala mʼmbali mwa nyanja,
6 Dziko la mʼmbali mwa nyanja, kumene kumakhala Akereti,
7 Malowa adzakhala a anthu otsala a nyumba ya Yuda;
8 “Ndamva kunyoza kwa Mowabu
9 Choncho, pali Ine Wamoyo,”
10 Ichi ndi chimene adzalandire chifukwa cha kunyada kwawo,
11 Yehova adzawachititsa mantha kwambiri
12 “Inunso anthu a ku Kusi,
13 Yehova adzatambasulira dzanja lake kumpoto
14 Nkhosa ndi ngʼombe zidzagona pansi kumeneko,
15 Umenewu ndiye mzinda wosasamala