1 Tsoka kwa mzinda wa anthu opondereza,
2 Sumvera aliyense,
3 Akuluakulu ake ali ngati mikango yobuma,
4 Aneneri ake ndi odzikuza;
5 Yehova amene ali pakati pawo ndi wolungama;
6 “Ndachotseratu mitundu ya anthu;
7 Ndinati,
8 Choncho mundidikire,” akutero Yehova,
9 “Pamenepo ndidzayeretsa milomo ya anthu a mitundu yonse
10 Kuchokera kutsidya kwa mitsinje ya ku Kusi
11 Tsiku limenelo simudzachita manyazi
12 Koma ndidzasiya pakati panu
13 Aisraeli otsala sadzachitanso zolakwika;
14 Imba, iwe mwana wamkazi wa Ziyoni;
15 Yehova wachotsa chilango chako,
16 Pa tsiku limenelo adzanena kwa Yerusalemu kuti,
17 Yehova Mulungu wako ali pakati pako,
18 “Ndidzakuchotserani zowawa
19 Taonani, nthawi imeneyo ndidzathana ndi
20 Pa nthawi imeneyo ndidzakusonkhanitsani;