1 Yehova anayankhula ndi Zefaniya mwana wa Kusi, mwana wa Gedaliya, mwana wa Amariya, mwana wa Hezekiya pa nthawi ya Yosiya, mwana wa Amoni, mfumu ya Yuda.
2 “Ndidzawononga kotheratu zinthu zonse
3 “Ndidzawononga anthu pamodzi ndi nyama zomwe;
4 Ndidzatambasula dzanja langa pa Yuda
5 amene amagwada pa madenga a nyumba zawo
6 amene abwerera mʼmbuyo osatsata Yehova,
7 Khalani chete pamaso pa Ambuye Yehova,
8 Pa tsiku la nsembe ya Yehova
9 Pa tsiku limenelo ndidzalanga
10 “Pa tsiku limenelo,” akutero Yehova,
11 Lirani mwachisoni, inu amene mumakhala kumene kuli msika;
12 Pa nthawi imeneyo ndidzafufuzafufuza mu Yerusalemu ndi nyale
13 Chuma chawo chidzafunkhidwa,
14 Tsiku lalikulu la Yehova layandikira,
15 Tsiku limenelo lidzakhala la ukali,
16 Tsiku loliza lipenga ndi la mfuwu wankhondo,
17 Ndidzabweretsa msautso pa anthu
18 Ngakhale siliva wawo kapena golide wawo