1 Pemphero la mneneri Habakuku potsata mayimbidwe a Sigionoti.
2 Inu Yehova, ndamva za kutchuka kwanu;
3 Mulungu anabwera kuchokera ku Temani,
4 Kuwala kwa ulemerero wake kunali ngati kutuluka kwa dzuwa;
5 Patsogolo pake pankagwa mliri;
6 Iye anayimirira ndi kugwedeza dziko lapansi;
7 Ndinaona matenti a ku Kusani ali pa mavuto,
8 Inu Yehova, kodi munakwiyira mitsinje?
9 Munasolola uta wanu mʼchimake,
10 mapiri anakuonani ndipo anagwedezeka.
11 Dzuwa ndi mwezi zinayima chilili mlengalenga,
12 Munayendayenda mʼdziko lapansi muli ndi ukali,
13 Munapita kukalanditsa anthu anu,
14 Ndi mkondo wake womwe munalasa mtsogoleri wake
15 Munapondaponda pa nyanja ndi akavalo anu,
16 Ndinamva ndipo mtima wanga unagunda kwambiri,
17 Ngakhale mtengo wa mkuyu usachite maluwa,
18 komabe ine ndidzakondwera mwa Yehova,
19 Ambuye Yehova ndiye mphamvu yanga;