1 Ndidzakhala pa malo anga aulonda,
2 Tsono Yehova anandiyankha, nati:
3 Pakuti masomphenyawa akudikira nthawi yake;
4 “Taona, mdani wadzitukumula;
5 Ndithu, wasokonezeka ndi vinyo;
6 “Kodi onse ogwidwawo sadzamunyoza ndi kumunyogodola ponena kuti,
7 Kodi angongole ako sadzakuwukira mwadzidzidzi?
8 Pakuti unafunkha mitundu yambiri ya anthu,
9 “Tsoka kwa amene amalemera ndi chuma chochipeza mwachinyengo,
10 Wakonzekera kuwononga mitundu yambiri ya anthu,
11 Mwala pa khoma udzafuwula,
12 “Tsoka kwa amene amanga mzinda pokhetsa magazi
13 Kodi Yehova Wamphamvuzonse sanatsimikize
14 Pakuti dziko lapansi lidzadzaza ndi chidziwitso cha ulemerero wa Yehova,
15 “Tsoka kwa amene amamwetsa anzake zakumwa zoledzeretsa,
16 Udzachita manyazi mʼmalo mokhala ndi ulemerero.
17 Udzathedwa nzeru ndi chiwawa chimene unachita ku Lebanoni,
18 “Kodi fano lili ndi phindu lanji, poti analisema ndi munthu,
19 Tsoka kwa amene amawuza mtengo kuti, ‘Khala wamoyo!’
20 Koma Yehova ali mʼNyumba yake yopatulika;