Habacuque 1

NYA

1 Uthenga umene mneneri Habakuku analandira mʼmasomphenya.

2 Kodi inu Yehova, ndidzakhala ndikukupemphani thandizo kwa nthawi yayitali motani,

3 Chifukwa chiyani mukundionetsa zinthu zoyipa?

4 Kotero malamulo anu atha mphamvu,

5 “Yangʼanani pakati pa mitundu ya anthu, ndipo penyetsetsani,

6 Pakuti taonani, Ine ndikuwutsa Ababuloni,

7 Iwowa ndi anthu ochititsa mantha, ndipo ndi owopsa;

8 Akavalo awo ndi aliwiro kwambiri kupambana akambuku

9 onse akubwera atakonzekera zachiwawa.

10 Akunyoza mafumu

11 Kenaka amasesa mofulumira ngati mphepo nʼkumangopitirirabe,

12 Inu Yehova, kodi sindinu wachikhalire?

13 Maso anu ndi oyera kwambiri safuna kuona choyipa;

14 Mwasandutsa anthu kukhala ngati nsomba zamʼnyanja,

15 Mdani wawo woyipa amakoka anthu onse ndi mbedza,

16 Choncho iye amaperekera nsembe ukonde wake

17 Kodi iye azipitirabe kugwiritsa ntchito makoka akewo,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado