1 Uthenga umene mneneri Habakuku analandira mʼmasomphenya.
2 Kodi inu Yehova, ndidzakhala ndikukupemphani thandizo kwa nthawi yayitali motani,
3 Chifukwa chiyani mukundionetsa zinthu zoyipa?
4 Kotero malamulo anu atha mphamvu,
5 “Yangʼanani pakati pa mitundu ya anthu, ndipo penyetsetsani,
6 Pakuti taonani, Ine ndikuwutsa Ababuloni,
7 Iwowa ndi anthu ochititsa mantha, ndipo ndi owopsa;
8 Akavalo awo ndi aliwiro kwambiri kupambana akambuku
9 onse akubwera atakonzekera zachiwawa.
10 Akunyoza mafumu
11 Kenaka amasesa mofulumira ngati mphepo nʼkumangopitirirabe,
12 Inu Yehova, kodi sindinu wachikhalire?
13 Maso anu ndi oyera kwambiri safuna kuona choyipa;
14 Mwasandutsa anthu kukhala ngati nsomba zamʼnyanja,
15 Mdani wawo woyipa amakoka anthu onse ndi mbedza,
16 Choncho iye amaperekera nsembe ukonde wake
17 Kodi iye azipitirabe kugwiritsa ntchito makoka akewo,