1 Tsoka kwa mzinda wopha anthu,
2 Kulira kwa zikwapu,
3 Kuthamanga kwa anthu okwera pa akavalo,
4 Zonsezi ndi chifukwa cha zilakolako za mkazi wachiwerewere,
5 Yehova Wamphamvuzonse akuti,
6 Ndidzakuthira zonyansa,
7 Onse amene adzakuona adzakuthawa ndipo adzati,
8 Kodi ndiwe wopambana Tebesi,
9 Mphamvu zake zinali Kusi ndi Igupto,
10 Komabe anthu a ku Tebesi anagwidwa
11 Iwenso Ninive udzaledzera;
12 Malo ako onse otetezedwa ali ngati mitengo ya mkuyu
13 Tayangʼana ankhondo ako,
14 Tungani madzi woti mudzamwe nthawi ya kuzunguliridwa kwanu,
15 Kumeneko moto udzakupserezani;
16 Mwachulukitsa chiwerengero cha anthu a malonda anu
17 Akalonga ako ali ngati dzombe,
18 Iwe mfumu ya ku Asiriya,
19 Palibe chimene chingachize bala lako;