Naum 3

NYA

1 Tsoka kwa mzinda wopha anthu,

2 Kulira kwa zikwapu,

3 Kuthamanga kwa anthu okwera pa akavalo,

4 Zonsezi ndi chifukwa cha zilakolako za mkazi wachiwerewere,

5 Yehova Wamphamvuzonse akuti,

6 Ndidzakuthira zonyansa,

7 Onse amene adzakuona adzakuthawa ndipo adzati,

8 Kodi ndiwe wopambana Tebesi,

9 Mphamvu zake zinali Kusi ndi Igupto,

10 Komabe anthu a ku Tebesi anagwidwa

11 Iwenso Ninive udzaledzera;

12 Malo ako onse otetezedwa ali ngati mitengo ya mkuyu

13 Tayangʼana ankhondo ako,

14 Tungani madzi woti mudzamwe nthawi ya kuzunguliridwa kwanu,

15 Kumeneko moto udzakupserezani;

16 Mwachulukitsa chiwerengero cha anthu a malonda anu

17 Akalonga ako ali ngati dzombe,

18 Iwe mfumu ya ku Asiriya,

19 Palibe chimene chingachize bala lako;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado