1 Wodzathira nkhondo akubwera
2 Yehova adzabwezeretsa ulemerero wa Yakobo
3 Zishango za ankhondo ake ndi zofiira;
4 Magaleta akuthamanga mʼmisewu
5 Iye akuyitanitsa asilikali ake wolemekezeka,
6 Atsekula zipata zotchinga madzi a mu mtsinje
7 Zatsimikizika kuti mzinda
8 Ninive ali ngati dziwe,
9 Funkhani siliva!
10 Iye wawonongedwa, wafunkhidwa ndipo wavulidwa!
11 Kodi tsopano dzenje la mikango lili kuti,
12 Mkango waumuna unkapha nyama yokwanira ana ake
13 Yehova Wamphamvuzonse akuti,