1 Uthenga wonena za Ninive. Buku la masomphenya a Nahumu wa ku Elikosi.
2 Yehova ndi Mulungu wansanje
3 Yehova sakwiya msanga koma ndi wa mphamvu yayikulu;
4 Amalamulira nyanja ndipo imawuma;
5 Mapiri amagwedera pamaso pake
6 Ndani angathe kuyima pamaso pake Iye akalusa?
7 Yehova ndi wabwino,
8 koma ndi madzi achigumula choopsa
9 Chiwembu chilichonse chimene akukonzekera kumuchitira Yehova
10 Iwo adzakodwa mu ziyangoyango za minga
11 Kwa iwe, Ninive, kunachokera munthu wa cholinga choyipa,
12 Yehova akuti,
13 Tsopano ndidzathyola goli lake pa khosi lako
14 Yehova walamulira za iwe, Ninive kuti,
15 Taonani, pa phiripo,