1 Tsoka ine!
2 Anthu opembedza atha mʼdziko;
3 Manja awo onse ndi aluso pochita zoyipa;
4 Munthu wabwino kwambiri pakati pawo ali ngati mtengo waminga,
5 Usadalire mnansi;
6 Pakuti mwana wamwamuna akunyoza abambo ake,
7 Koma ine ndikudikira Yehova mwachiyembekezo,
8 Iwe mdani wanga, usandiseke!
9 Ndidzapirira mkwiyo wa Yehova,
10 Ndipo mdani wanga adzaona zimenezi
11 Idzafika nthawi yomanganso makoma anu,
12 Nthawi imeneyo anthu adzabwera kwa inu
13 Dziko lapansi lidzasanduka chipululu
14 Wetani anthu anu ndi ndodo yanu yowateteza,
15 “Ndidzawaonetsa zodabwitsa zanga,
16 Mitundu ya anthu idzaona zimenezi ndipo idzachita manyazi,
17 Adzabwira fumbi ngati njoka,
18 Kodi alipo Mulungu wofanana nanu,
19 Inu mudzatichitiranso chifundo;
20 Mudzakhala wokhulupirika kwa Yakobo,