Miquéias 7

NYA

1 Tsoka ine!

2 Anthu opembedza atha mʼdziko;

3 Manja awo onse ndi aluso pochita zoyipa;

4 Munthu wabwino kwambiri pakati pawo ali ngati mtengo waminga,

5 Usadalire mnansi;

6 Pakuti mwana wamwamuna akunyoza abambo ake,

7 Koma ine ndikudikira Yehova mwachiyembekezo,

8 Iwe mdani wanga, usandiseke!

9 Ndidzapirira mkwiyo wa Yehova,

10 Ndipo mdani wanga adzaona zimenezi

11 Idzafika nthawi yomanganso makoma anu,

12 Nthawi imeneyo anthu adzabwera kwa inu

13 Dziko lapansi lidzasanduka chipululu

14 Wetani anthu anu ndi ndodo yanu yowateteza,

15 “Ndidzawaonetsa zodabwitsa zanga,

16 Mitundu ya anthu idzaona zimenezi ndipo idzachita manyazi,

17 Adzabwira fumbi ngati njoka,

18 Kodi alipo Mulungu wofanana nanu,

19 Inu mudzatichitiranso chifundo;

20 Mudzakhala wokhulupirika kwa Yakobo,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado