Miquéias 6

NYA

1 Tamverani zimene Yehova akunena:

2 Imvani mlandu wa Yehova, inu mapiri;

3 “Anthu anga, kodi ndakuchitirani chiyani?

4 Ine ndinakutulutsani ku dziko la Igupto

5 Anthu anga, kumbukirani

6 Kodi ndidzatenga chiyani kupita nacho pamaso pa Yehova

7 Kodi Yehova adzakondwera ndi nkhosa zazimuna 1,000,

8 Munthu iwe, Yehova wakuonetsa kale chimene chili chabwino.

9 Tamverani! Yehova akuyitana anthu okhala mu mzinda

10 Inu anthu oyipa, kodi Ine nʼkuyiwala

11 Kodi ndimutenge ngati wosalakwa munthu amene ali ndi sikelo yachinyengo,

12 Anthu ake olemera amachita zachiwawa;

13 Choncho, ndayamba kukuwonongani,

14 Mudzadya, koma simudzakhuta;

15 Mudzadzala, koma simudzakolola.

16 Inu mwatsatira malangizo a Omuri

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado