1 Tamverani zimene Yehova akunena:
2 Imvani mlandu wa Yehova, inu mapiri;
3 “Anthu anga, kodi ndakuchitirani chiyani?
4 Ine ndinakutulutsani ku dziko la Igupto
5 Anthu anga, kumbukirani
6 Kodi ndidzatenga chiyani kupita nacho pamaso pa Yehova
7 Kodi Yehova adzakondwera ndi nkhosa zazimuna 1,000,
8 Munthu iwe, Yehova wakuonetsa kale chimene chili chabwino.
9 Tamverani! Yehova akuyitana anthu okhala mu mzinda
10 Inu anthu oyipa, kodi Ine nʼkuyiwala
11 Kodi ndimutenge ngati wosalakwa munthu amene ali ndi sikelo yachinyengo,
12 Anthu ake olemera amachita zachiwawa;
13 Choncho, ndayamba kukuwonongani,
14 Mudzadya, koma simudzakhuta;
15 Mudzadzala, koma simudzakolola.
16 Inu mwatsatira malangizo a Omuri