1 Mwana wanga, mvera mawu anga;
2 Utsate malamulo anga ndipo udzakhala ndi moyo;
3 Uchite ngati wawamangirira pa zala zako,
4 Nzeru uyiwuze kuti, “Iwe ndiwe mlongo wanga,”
5 Zidzakuteteza kwa mkazi wachigololo
6 Tsiku lina pa zenera la nyumba yanga
7 Ndinaona pakati pa anthu opusa,
8 Iye ankayenda njira yodutsa pafupi ndi nyumba ya mkaziyo,
9 Inali nthawi yachisisira madzulo,
10 Ndipo mkaziyo anadzakumana naye,
11 (Mkaziyo ndi wolongolola ndiponso nkhutukumve,
12 Mwina umupeza pa msewu, mwina umupeza pa msika,
13 Tsono amagwira mnyamatayo ndi kupsompsona
14 “Ndinayenera kupereka nsembe zachiyanjano.
15 Choncho ndinabwera kudzakumana nawe;
16 Pa bedi panga ndayalapo
17 Pa bedi panga ndawazapo zonunkhira
18 Bwera, tiye tikhale malo amodzi kukondwerera chikondi mpaka mmawa;
19 Mwamuna wanga kulibe ku nyumbako;
20 Anatenga thumba la ndalama
21 Ndi mawu ake onyengerera amamukakamiza mnyamatayo;
22 Nthawi yomweyo chitsiru chimamutsatira mkaziyo
23 mpaka muvi utalasa chiwindi chake,
24 Tsono ana inu, ndimvereni;
25 Musatengeke mtima ndi njira za mkazi ameneyu;
26 Paja iye anagwetsa anthu ambiri;
27 Nyumba yake ndi njira yopita ku manda,