1 Kodi nzeru sikuyitana?
2 Nzeru imayima pa zitunda mʼmbali mwa njira,
3 Imafuwula pafupi ndi zipata zolowera mu mzinda,
4 Inu anthu, ndikuyitana inu;
5 Inu amene simudziwa kanthunu khalani ochenjera;
6 Mverani, pakuti ndikukuwuzani zinthu zofunika kwambiri;
7 Pakamwa panga pamayankhula zoona
8 Mawu onse a pakamwa panga ndi olungama;
9 Kwa anthu ozindikira, mawu anga onse ndi woona;
10 Landirani malangizo anga mʼmalo mwa siliva,
11 Paja nzeru ndi yabwino kwambiri kuposa miyala yamtengowapatali,
12 Ine nzeru, ndimakhala pamodzi ndi kuchenjera.
13 Kuopa Yehova ndiko kudana ndi zoyipa.
14 Ndine mwini uphungu ndi maganizo abwino;
15 Ndine amene ndimathandiza mafumu kulamulira.
16 Ndine amene ndimathandiza akalonga polamula.
17 Ndimakonda amene amandikonda,
18 Ine ndili ndi chuma ndi ulemu,
19 Chipatso changa ndi chabwino kuposa golide, ngakhale golide wosalala;
20 Ndimachita zinthu zolungama.
21 Ndimapereka chuma kwa amene amandikonda
22 “Yehova anandilenga ine nzeru monga ntchito yake yoyamba.
23 Ndinapangidwa kalekalelo,
24 Nyanja, akasupe odzaza ndi madzi,
25 Mapiri asanakhazikitsidwe pa malo awo,
26 lisanalengedwe dziko lapansi ndi minda yake;
27 Ine ndinalipo pamene Yehova ankakhazikitsa mlengalenga,
28 pamene anakhazikitsa mitambo ya mlengalenga
29 pamene anayikira nyanja malire
30 Tsono ine ndinali pambali pake ngati mmisiri;
31 Ndinkasangalala ndi dziko lake lonse
32 “Ndiye tsono ana inu, ndimvereni;
33 Mverani malangizo anga kuti mukhale ndi nzeru;
34 Wodala munthu amene amandimvera,
35 Paja aliyense amene apeza ine wapeza moyo
36 Koma amene alephera kundipeza, amadzipweteka yekha;