Provérbios 5

NYA

1 Mwana wanga, mvetsera bwino za nzeru zimene ndikukuwuzazi,

2 kuti uthe kuchita zinthu mochenjera ndi mwanzeru

3 Pakuti mkazi wachigololo ali ndi mawu okoma ngati uchi.

4 koma kotsirizira kwake ngowawa ngati ndulu;

5 Mapazi ake amatsikira ku imfa;

6 Iye saganizirapo za njira ya moyo;

7 Tsopano ana inu, mundimvere;

8 Uziyenda kutali ndi mkazi wotereyo,

9 kuopa kuti ungadzalanditse ulemerero wako kwa anthu ena;

10 kapenanso alendo angadyerere chuma chako

11 Potsiriza pa moyo wako udzabuwula,

12 Ndipo udzati, “Mayo ine, ndinkadana ndi kusunga mwambo!

13 Sindinamvere aphunzitsi anga

14 Ine ndatsala pangʼono kuti ndiwonongeke

15 Imwa madzi a mʼchitsime chakochako,

16 Kodi akasupe ako azingosefukira mʼmisewu?

17 Mitsinjeyo ikhale ya iwe wekha,

18 Yehova adalitse kasupe wako,

19 Iye uja ali ngati mbalale yayikazi yokongola ndiponso ngati gwape wa maonekedwe abwino.

20 Mwana wanga, nʼchifukwa chiyani ukukopeka ndi mkazi wachigololo?

21 Pakuti mayendedwe onse a munthu Yehova amawaona,

22 Ntchito zoyipa za munthu woyipa zimamukola yekha;

23 Iye adzafa chifukwa chosowa mwambo,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado