Provérbios 30

NYA

1 Nawa mawu a Aguri mwana wa Yake wa ku Masa:

2 “Ine ndine munthu wopusa kuposa anthu onse;

3 Sindinaphunzire nzeru,

4 Kodi ndani anakwera kumwamba ndi kutsikako?

5 “Mawu ali wonse a Mulungu ndi opanda cholakwika;

6 Usawonjezepo kanthu pa mawu ake,

7 “Inu Yehova, ndikukupemphani zinthu ziwiri

8 Choyamba, mundichotsere kutali nane mabodza ndi chinyengo.

9 kuopa kuti ndikakhuta kwambiri ndingayambe kukukanani,

10 “Usamusinjirire wantchito kwa mbuye wake

11 “Alipo ena amene amatemberera abambo awo,

12 Pali ena amene amadziyesa okha oyera mtima

13 Pali ena ndi odzitukumula kwambiri,

14 Pali ena amene mano awo ali ngati malupanga

15 “Msundu uli ndi ana aakazi awiri

16 Manda, mkazi wosabala,

17 Aliyense amene amanyoza abambo ake,

18 Pali zinthu zitatu zimene zimandidabwitsa,

19 Ndipo ndi izi: mmene chiwulukira chiwombankhanga mlengalenga;

20 Umu ndi mʼmene mkazi amachitira atachita chigololo:

21 Pali zinthu zitatu zimene zimanjenjemeretsa dziko lapansi,

22 Kapolo amene wasanduka mfumu,

23 mkazi wonyozeka akakwatiwa

24 Pali zinthu zinayi zingʼonozingʼono pa dziko lapansi,

25 Nyerere zili ngati anthu opanda mphamvu,

26 mbira zili ngati anthu opanda mphamvu

27 dzombe lilibe mfumu,

28 Buluzi ungathe kumugwira mʼmanja

29 “Pali zinthu zitatu zimene zimayenda chinyachinya,

30 Mkango umene uli wamphamvu kuposa nyama zonse,

31 Tambala woyenda chinyachinya, mbuzi yayimuna,

32 “Ngati wakhala ukupusa ndi kumadzikweza wekha,

33 Paja pakutha mkaka mafuta amapangidwa,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado