1 Munthu amene amawumitsabe khosi lake atadzudzulidwa kwambiri,
2 Anthu olungama akamalamulira mʼdziko anthu amakondwa,
3 Munthu amene amakonda nzeru amasangalatsa abambo ake,
4 Mfumu imalimbitsa dziko poweruza mwachilungamo,
5 Munthu woshashalika mnzake,
6 Munthu woyipa amakodwa ndi machimo ake,
7 Munthu wolungama amasamalira anthu osauka,
8 Anthu onyoza atha kuwutsa ziwawa mu mzinda,
9 Ngati munthu wanzeru atsutsana ndi chitsiru,
10 Anthu okhetsa magazi amadana ndi munthu wangwiro
11 Munthu wopusa amaonetsa mkwiyo wake,
12 Ngati wolamulira amvera zabodza,
13 Munthu wosauka ndi munthu wopondereza anzake amafanana pa kuti:
14 Ngati mfumu iweruza osauka moyenera,
15 Ndodo ndi chidzudzulo zimapatsa nzeru
16 Oyipa akamalamulira zoyipa zimachuluka,
17 Umulange mwana wako ndipo adzakupatsa mtendere
18 Ngati uthenga wochokera kwa Yehova supezeka anthu amangochita zofuna zawo;
19 Munthu wantchito sangalangizidwe ndi mawu okha basi;
20 Ngakhale munthu wa uchitsiru nʼkuti ndiponi popeza chikhulupiriro chilipo
21 Ngati munthu asasatitsa wantchito wake kuyambira ali mwana,
22 Munthu wamkwiyo amayambitsa mikangano,
23 Kunyada kwa munthu kudzamutsitsa,
24 Woyenda ndi munthu wakuba ndi mdani wa moyo wake womwe;
25 Kuopa munthu kudzakhala ngati msampha,
26 Anthu ambiri amafunitsitsa kuti wolamulira awakomere mtima,
27 Anthu olungama amanyansidwa ndi anthu achinyengo;