1 Munthu woyipa amathawa ngakhale palibe wina womuthamangitsa,
2 Pamene mʼdziko muli kuwukirana, dzikolo limakhala ndi olamulira ambiri,
3 Munthu wosauka amene amapondereza osauka anzake
4 Amene amakana malamulo amatamanda anthu oyipa,
5 Anthu oyipa samvetsa za chiweruzo cholungama,
6 Munthu wosauka wa makhalidwe abwino
7 Amene amasunga malamulo ndi mwana wozindikira zinthu,
8 Amene amachulukitsa chuma chake polandira chiwongoladzanja chochuluka
9 Wokana kumvera malamulo
10 Amene amatsogolera anthu olungama kuti ayende mʼnjira yoyipa
11 Munthu wolemera amadziyesa kuti ndi wanzeru,
12 Pamene olungama apambana pamakhala chikondwerero chachikulu;
13 Wobisa machimo ake sadzaona mwayi,
14 Ndi wodala munthu amene amaopa Yehova nthawi zonse,
15 Ngati mkango wobuma kapena chimbalangondo cholusa
16 Wolamulira amene samvetsa zinthu ndiye amakhala wankhanza
17 Munthu amene wapalamula mlandu wopha munthu
18 Amene amayenda mokhulupirika adzapulumutsidwa
19 Amene amalima mʼmunda mwake adzakhala ndi chakudya chochuluka,
20 Munthu wokhulupirika adzadalitsika kwambiri,
21 Kukondera si kwabwino,
22 Munthu wowumira amafunitsitsa kulemera
23 Amene amadzudzula mnzake potsiriza pake
24 Amene amabera abambo ake kapena amayi ake
25 Munthu wadyera amayambitsa mikangano,
26 Amene amadzidalira yekha ndi chitsiru,
27 Amene amapereka kwa osauka sadzasowa kanthu,
28 Pamene anthu oyipa apatsidwa ulamuliro anthu amabisala,