Provérbios 28

NYA

1 Munthu woyipa amathawa ngakhale palibe wina womuthamangitsa,

2 Pamene mʼdziko muli kuwukirana, dzikolo limakhala ndi olamulira ambiri,

3 Munthu wosauka amene amapondereza osauka anzake

4 Amene amakana malamulo amatamanda anthu oyipa,

5 Anthu oyipa samvetsa za chiweruzo cholungama,

6 Munthu wosauka wa makhalidwe abwino

7 Amene amasunga malamulo ndi mwana wozindikira zinthu,

8 Amene amachulukitsa chuma chake polandira chiwongoladzanja chochuluka

9 Wokana kumvera malamulo

10 Amene amatsogolera anthu olungama kuti ayende mʼnjira yoyipa

11 Munthu wolemera amadziyesa kuti ndi wanzeru,

12 Pamene olungama apambana pamakhala chikondwerero chachikulu;

13 Wobisa machimo ake sadzaona mwayi,

14 Ndi wodala munthu amene amaopa Yehova nthawi zonse,

15 Ngati mkango wobuma kapena chimbalangondo cholusa

16 Wolamulira amene samvetsa zinthu ndiye amakhala wankhanza

17 Munthu amene wapalamula mlandu wopha munthu

18 Amene amayenda mokhulupirika adzapulumutsidwa

19 Amene amalima mʼmunda mwake adzakhala ndi chakudya chochuluka,

20 Munthu wokhulupirika adzadalitsika kwambiri,

21 Kukondera si kwabwino,

22 Munthu wowumira amafunitsitsa kulemera

23 Amene amadzudzula mnzake potsiriza pake

24 Amene amabera abambo ake kapena amayi ake

25 Munthu wadyera amayambitsa mikangano,

26 Amene amadzidalira yekha ndi chitsiru,

27 Amene amapereka kwa osauka sadzasowa kanthu,

28 Pamene anthu oyipa apatsidwa ulamuliro anthu amabisala,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado