1 Usamanyadire za mawa,
2 Munthu wina akutamande, koma osati wekha;
3 Mwala ndi wolemera ndipo mchenganso ndi wolemera kwambiri,
4 Mkwiyo umadzetsa nkhanza ndipo kupsa mtima kumachititsa zoopsa.
5 Kudzudzula munthu poyera nʼkwabwino
6 Munthu amene amakukonda ngakhale akupweteke zili bwino,
7 Iye amene wakhuta amayipidwa ndi chisa cha uchi,
8 Munthu amene wasochera ku nyumba kwake,
9 Mafuta ndi zonunkhira zimasangalatsa mtima,
10 Usasiye bwenzi lako ndiponso bwenzi la abambo ako,
11 Mwana wanga, khala wanzeru, ndipo ukondweretse mtima wanga;
12 Munthu wochenjera akaona choopsa amabisala,
13 Utenge chovala cha munthu amene waperekera mlendo chikole;
14 Ngati munthu apatsa mnzake moni mofuwula mmamawa kwambiri,
15 Mkazi wolongolola ali ngati
16 Kumuletsa mkazi wotereyu zimenezi zili ngati kuletsa mphepo
17 Chitsulo chimanoledwa ndi chitsulo chinzake,
18 Amene amasamalira mtengo wamkuyu adzadya zipatso zake,
19 Monga momwe nkhope imaonekera mʼmadzi,
20 Manda sakhuta,
21 Siliva amasungunulira mu uvuni ndipo golide mʼngʼanjo,
22 Ngakhale utakonola chitsiru mu mtondo
23 Uzidziwe bwino nkhosa zako momwe zilili.
24 Paja chuma sichikhala mpaka muyaya,
25 Pamene udzu watha, msipu nʼkumera;
26 ana ankhosa adzakupatsani chovala
27 Mudzakhala ndi mkaka wambuzi wambiri