1 Ngati chisanu choti mbee nthawi yachilimwe kapena mvula nthawi yokolola,
2 Ngati timba wokhalira kuwuluka kapena namzeze wokhalira kuzungulirazungulira,
3 Mkwapulo ndi wokwapulira kavalo, chitsulo ndi cha mʼkamwa mwa bulu,
4 Usayankhe chitsiru monga mwa uchitsiru wake,
5 Koma nthawi zina umuyankhe monga mwa uchitsiru wake,
6 Kutuma chitsiru kuti akapereke uthenga
7 Monga miyendo ya munthu wolumala imene ilibe mphamvu
8 Kupereka ulemu kwa chitsiru
9 Monga umachitira mtengo waminga wobaya mʼdzanja la chidakwa
10 Munthu amene amalemba ntchito chitsiru chongoyendayenda,
11 Chitsiru chimene chimabwerezabwereza uchitsiru wake
12 Munthu wa uchitsiru aliko bwino popeza pali chiyembekezo
13 Munthu waulesi amati, “Mu msewu muli mkango,
14 Monga chitseko chimapita uku ndi uku pa zolumikizira zake,
15 Munthu waulesi akapisa dzanja lake mu mʼbale;
16 Munthu waulesi amadziyesa yekha wanzeru
17 Munthu wongolowera mikangano imene si yake
18 Monga munthu wamisala amene
19 ndi momwe alili munthu wonamiza mnzake,
20 Pakasowa nkhuni, moto umazima;
21 Monga alili makala pa moto wonyeka kapena mmene zimachitira nkhuni pa moto,
22 Mawu a munthu wamiseche ali ngati chakudya chokoma;
23 Monga mmene chiziro chimakutira chiwiya chadothi
24 Munthu wachidani amayankhula zabwino
25 Ngakhale wotereyu mawu ake ali okoma, koma usamukhulupirire,
26 Ngakhale amabisa chidani mochenjera,
27 Ngati munthu akumba dzenje, adzagweramo yekha;
28 Munthu wonama amadana ndi amene anawapweteka,