Provérbios 25

NYA

1 Iyi ndi miyambo inanso ya Solomoni, imene anthu a Hezekiya mfumu ya ku Yuda analemba.

2 Ulemerero wa Mulungu uli pa kubisa zinthu;

3 Monga momwe kwatalikira kumwamba ndi momwe kulili kuzama kwa dziko lapansi,

4 Chotsa zoyipa mʼsiliva

5 Chotsa munthu woyipa pamaso pa mfumu;

6 Usamadzikuze ukakhala pamaso pa mfumu,

7 paja ndi bwino kuti mfumu ichite kukuwuza kuti, “Bwera pamwamba pano,”

8 usafulumire kupita nacho ku bwalo la milandu

9 Kamba mlandu ndi mnansi wako,

10 kuopa kuti wina akamva mawu ako adzakuchititsa manyazi

11 Mawu amodzi woyankhulidwa moyenera

12 Kwa munthu womvetsa bwino, kudzudzula kwa munthu wanzeru kuli ngati ndolo zagolide

13 Wamthenga wodalirika ali ngati madzi ozizira pa nthawi yokolola

14 Munthu wonyadira mphatso imene sayipereka

15 Kupirira ndiye kumagonjetsa mfumu,

16 Ngati upeza uchi, ingodya okukwanira,

17 Uzipita kamodzikamodzi ku nyumba ya mnzako

18 Munthu wochitira mnzake umboni wonama,

19 Kudalira munthu wosankhulupirika pa nthawi ya mavuto,

20 Kuyimbira nyimbo munthu wachisoni

21 Ngati mdani wako ali ndi njala, mupatse chakudya kuti adye;

22 Pochita izi, udzamusenzetsa makala a moto pa mutu pake,

23 Monga momwe mphepo yampoto imabweretsera mvula,

24 Nʼkwabwino kukhala pa ngodya ya denga

25 Mthenga wabwino wochokera ku dziko lakutali

26 Munthu wolungama amene amagonjera munthu woyipa

27 Sibwino kudya uchi wambiri,

28 Munthu amene samatha kudziretsa

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado