1 Iyi ndi miyambo inanso ya Solomoni, imene anthu a Hezekiya mfumu ya ku Yuda analemba.
2 Ulemerero wa Mulungu uli pa kubisa zinthu;
3 Monga momwe kwatalikira kumwamba ndi momwe kulili kuzama kwa dziko lapansi,
4 Chotsa zoyipa mʼsiliva
5 Chotsa munthu woyipa pamaso pa mfumu;
6 Usamadzikuze ukakhala pamaso pa mfumu,
7 paja ndi bwino kuti mfumu ichite kukuwuza kuti, “Bwera pamwamba pano,”
8 usafulumire kupita nacho ku bwalo la milandu
9 Kamba mlandu ndi mnansi wako,
10 kuopa kuti wina akamva mawu ako adzakuchititsa manyazi
11 Mawu amodzi woyankhulidwa moyenera
12 Kwa munthu womvetsa bwino, kudzudzula kwa munthu wanzeru kuli ngati ndolo zagolide
13 Wamthenga wodalirika ali ngati madzi ozizira pa nthawi yokolola
14 Munthu wonyadira mphatso imene sayipereka
15 Kupirira ndiye kumagonjetsa mfumu,
16 Ngati upeza uchi, ingodya okukwanira,
17 Uzipita kamodzikamodzi ku nyumba ya mnzako
18 Munthu wochitira mnzake umboni wonama,
19 Kudalira munthu wosankhulupirika pa nthawi ya mavuto,
20 Kuyimbira nyimbo munthu wachisoni
21 Ngati mdani wako ali ndi njala, mupatse chakudya kuti adye;
22 Pochita izi, udzamusenzetsa makala a moto pa mutu pake,
23 Monga momwe mphepo yampoto imabweretsera mvula,
24 Nʼkwabwino kukhala pa ngodya ya denga
25 Mthenga wabwino wochokera ku dziko lakutali
26 Munthu wolungama amene amagonjera munthu woyipa
27 Sibwino kudya uchi wambiri,
28 Munthu amene samatha kudziretsa