1 Usachitire nsanje anthu oyipa,
2 pakuti mitima yawo imalingalira chiwawa,
3 Nyumba imamangidwa ndi anthu anzeru,
4 Munthu wodziwa zinthu angathe kudzaza zipinda zake
5 Munthu wodziwa zinthu ali ndi mphamvu yayikulu kuposa munthu wanyonga zambiri,
6 Pafunika malangizo kuti ukamenye nkhondo.
7 Nzeru ndi chinthu chapatali kwambiri kwa chitsiru;
8 Amene amakonzekera kuchita zoyipa
9 Kukonzekera kuchita za uchitsiru ndi tchimo,
10 Ngati utaya mtima nthawi ya mavuto ndiye kuti
11 Uwapulumutse amene akutengedwa kuti akaphedwe;
12 Ukanena kuti, “Koma ife sitinadziwe kanthu za izi,”
13 Mwana wanga, uzidya uchi popeza ndi wabwino;
14 Udziwe kuti nzeru ndi yoteronso pa moyo wako;
15 Usachite zachifwamba nyumba ya munthu wolungama ngati munthu woyipa.
16 paja munthu wolungama akagwa kasanu nʼkawiri amadzukiriranso.
17 Usamakondwera ndi kugwa kwa mdani wako.
18 Kuopa kuti Yehova ataziona zimenezi nayipidwa nazo,
19 Usavutike mtima chifukwa cha anthu ochita zoyipa
20 paja munthu woyipa alibe tsogolo.
21 Mwana wanga, uziopa Yehova ndi mfumu,
22 awiri amenewa amagwetsa tsoka mwadzidzidzi.
23 Malangizo enanso a anthu anzeru ndi awa:
24 Aliyense amene amawuza munthu wolakwa kuti, “Iwe ndi munthu wosalakwa,”
25 Koma olanga anthu oyipa zinthu zidzawayendera bwino
26 Woyankhula mawu owona
27 Ugwiriretu ntchito zako zonse,
28 Usakhale mboni yotsutsa mnzako popanda chifukwa,
29 Usanene kuti, “Ine ndidzamuchitira iye monga momwe wandichitira ine;
30 Ndinkayenda mʼmbali mwa munda wa munthu waulesi
31 Ndinapeza kuti paliponse mʼmundamo munali mutamera minga,
32 Tsono nditaona ndinayamba kuganizira mu mtima mwanga
33 Ukati, “Bwanji ndigone pangʼono,” kapena “Ndiwodzereko pangʼono,”
34 umphawi udzafika pa iwe ngati mbala