1 Ngati ukhala pansi kuti udye pamodzi ndi wolamulira,
2 ngati ndiwe munthu wadyera
3 Usasirire zakudya zake,
4 Usadzitopetse wekha ndi kufuna chuma,
5 Ukangoti wachipeza chumacho uwona posachedwa kuti palibepo.
6 Usadye chakudya cha munthu waumbombo,
7 paja iye ndi munthu amene
8 Udzasanza zimene wadyazo
9 Usayankhule munthu wopusa akumva,
10 Usasunthe mwala wa mʼmalire akalekale
11 paja Mpulumutsi wawo ndi wamphamvu;
12 Mtima wako uzikhala pa malangizo
13 Usaleke kumulangiza mwana;
14 Ukamukwapula ndi tsatsa
15 Mwana wanga, ngati mtima wako ukhala wanzeru,
16 Mtima wanga udzakondwera
17 Mtima wako usachite nsanje ndi anthu ochimwa,
18 Ndithu za mʼtsogolo zilipo
19 Tamvera mwana wanga, ndipo ukhale wanzeru,
20 Usakhale pakati pa anthu amene amaledzera
21 Paja anthu oledzera ndi adyera amadzakhala amphawi
22 Mvera abambo ako amene anakubala,
23 Gula choonadi ndipo usachigulitse;
24 Abambo a munthu wolungama ali ndi chimwemwe chachikulu;
25 Abambo ndi amayi ako asangalale;
26 Mwana wanga, undikhulupirire
27 Paja mkazi wachiwerewere ali ngati dzenje lozama;
28 Amabisala ngati mbala yachifwamba,
29 Ndani ali ndi tsoka? Ndani ali ndi chisoni?
30 Ndi amene amakhalitsa pa mowa,
31 Usatengeke mtima ndi kufiira kwa vinyo,
32 Potsiriza pake amaluma ngati njoka,
33 Maso ako adzaona zinthu zachilendo
34 Udzakhala ngati munthu amene ali gone pakati pa nyanja,
35 Iwe udzanena kuti, “Anandimenya, koma sindinapwetekedwe!