Provérbios 22

NYA

1 Mbiri yabwino ndi yofunika kuposa chuma chambiri;

2 Wolemera ndi wosauka ndi ofanana;

3 Munthu wochenjera akaona choopsa amabisala,

4 Mphotho ya munthu wodzichepetsa

5 Mʼnjira za anthu oyipa muli minga ndi misampha,

6 Mwana muzimuphunzitsa njira yake,

7 Wolemera amalamulira wosauka,

8 Amene amafesa zoyipa amakolola mavuto,

9 Amene ali ndi diso lachifundo adzadalitsika,

10 Chotsani munthu wonyoza, ndipo kukangana kudzatha;

11 Amene amakonda kukhala woyera mtima ndi kumayankhula mawu abwino,

12 Maso a Yehova amakhala pa anthu odziwa bwino zinthu,

13 Munthu waulesi amati,

14 Pakamwa pa mkazi wachigololo pali ngati dzenje lozama;

15 Uchitsiru umakhala mu mtima mwa mwana,

16 Amene amapondereza anthu osauka kuti awonjezere chuma chake,

17 Utchere khutu lako ndipo umvere mawu anzeru;

18 Zidzakhala zokondweretsa ngati uzisunga mu mtima mwako

19 Ndakuphunzitsa zimenezi lero

20 Kodi suja ndinakulembera malangizo makumi atatu

21 malangizo okudziwitsa zolungama

22 Mʼmphawi usamubere chifukwa ndi osauka,

23 pakuti Yehova adzawateteza pa mlandu wawo

24 Usapalane naye ubwenzi munthu wosachedwa kupsa mtima

25 kuopa kuti iwe ungadzaphunzire njira zake

26 Usakhale munthu wopereka chikole

27 ngati ulephera kupeza njira yolipirira

28 Usasunthe mwala wamʼmalire akalekale

29 Kodi ukumuona munthu waluso pa ntchito yake?

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado