1 Mtima wa mfumu uli ngati mtsinje wamadzi mʼdzanja la Yehova;
2 Makhalidwe a munthu amaoneka olungama kwa mwini wakeyo,
3 Za chilungamo ndi zolondola
4 Maso odzikuza ndi mtima wonyada,
5 Zolinga za munthu wakhama zimachulukitsa zinthu zake;
6 Chuma chochipeza ndi mawu onyenga ndi chosakhalitsa
7 Chiwawa cha anthu oyipa chidzawawononga,
8 Njira ya munthu wolakwa ndi yokhotakhota,
9 Nʼkwabwino kukhala wekha pa ngodya ya denga la nyumba,
10 Munthu woyipa amalakalaka zoyipa;
11 Munthu wonyoza akalangidwa, anthu opusa amapeza nzeru;
12 Zolingalira za munthu woyipa nʼzosabisika pamaso pa Yehova,
13 Amene atsekera mʼkhutu mwake wosauka akamalira,
14 Mphatso yoperekedwa mseri imathetsa mkwiyo,
15 Chilungamo chikachitika anthu olungama amasangalala,
16 Munthu amene amachoka pa njira ya anthu anzeru
17 Aliyense wokonda zisangalalo adzasanduka mʼmphawi,
18 Anthu oyipa adzakhala chowombolera cha anthu olungama
19 Nʼkwabwino kukhala mʼchipululu
20 Munthu wanzeru samwaza chuma chake,
21 Amene amatsata chilungamo ndi kukhulupirika,
22 Munthu wanzeru amagonjetsa mzinda wa anthu amphamvu
23 Amene amagwira pakamwa pake ndi lilime lake
24 Munthu wonyada ndi wodzikuza amamutcha, “Mnyodoli,”
25 Chilakolako cha munthu waulesi chidzamupha yekha
26 Tsiku lonse anthu oyipa amasirira zambiri,
27 Nsembe ya anthu oyipa imamunyansa Yehova,
28 Mboni yonama idzawonongeka,
29 Munthu woyipa amafuna kudzionetsa ngati wolimba mtima,
30 Palibe nzeru, palibe kumvetsa bwino, palibenso uphungu,
31 Kavalo amamukonzera tsiku la nkhondo,