Provérbios 3

NYA

1 Mwana wanga, usayiwale malangizo anga,

2 Ukatero zaka za moyo wako zidzachuluka

3 Makhalidwe ochitira ena chifundo ndi owonetsa kukhulupirika asakuchokere.

4 Ukatero udzapeza kuyanja ndi mbiri yabwino

5 Uzikhulupirira Yehova ndi mtima wako wonse

6 Pa zochita zako zonse uvomereze kuti Mulungu alipo,

7 Usamadzione ngati wa nzeru.

8 Ukatero thupi lako lidzakhala la moyo wabwino

9 Uzilemekeza Yehova ndi chuma chako chonse;

10 Ukatero nkhokwe zako zidzadzaza ndi zinthu zambiri,

11 Mwana wanga usanyoze malangizo a Yehova,

12 Paja Yehova amadzudzula amene amamukonda,

13 Wodala munthu amene wapeza nzeru,

14 pakuti phindu la nzeru ndi labwino kuposa la siliva,

15 Nzeru ndi yoposa miyala yamtengowapatali;

16 Mʼdzanja lake lamanja muli moyo wautali;

17 Njira zake ndi njira zosangalatsa,

18 Nzeru ili ngati mtengo wopatsa moyo kwa oyigwiritsitsa;

19 Yehova anakhazikitsa dziko lapansi pogwiritsa ntchito nzeru.

20 Mwa nzeru zake Yehova anatumphutsa madzi kuchokera mʼnthaka

21 Mwana wanga usunge nzeru yeniyeni ndi khalidwe lomalingarira zinthu bwino.

22 Zimenezi zidzakupatsa moyo,

23 Choncho udzayenda pa njira yako mosaopa kanthu,

24 pamene ugona pansi, sudzachita mantha;

25 Usaope tsoka lobwera mwadzidzidzi

26 pakuti Yehova adzakulimbitsa mtima

27 Usaleke kuchitira zabwino amene ayenera kulandira zabwino,

28 Usanene kwa mnansi wako kuti,

29 Usamukonzere chiwembu mnansi wako,

30 Usakangane ndi munthu wopanda chifukwa

31 Usachite naye nsanje munthu wachiwawa

32 Pakuti Yehova amanyansidwa ndi munthu woyipa

33 Yehova amatemberera nyumba ya munthu woyipa,

34 Anthu onyoza, Iye amawanyoza,

35 Anthu anzeru adzalandira ulemu,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado