Provérbios 2

NYA

1 Mwana wanga, ngati ulandira mawu anga

2 ndiponso kutchera khutu lako ku nzeru

3 ngati upempha kuti uzindikire zinthu

4 ngati ufunafuna nzeruyo ngati siliva

5 ndiye udzamvetsa bwino tanthauzo la kuopa Yehova;

6 Pakuti Yehova ndiye amapereka nzeru,

7 Anthu olungama zinthu zimawayendera bwino chifukwa Yehova amakhala nawo.

8 pakuti ndiye mlonda wa njira zolungama.

9 Choncho udzamvetsa tanthauzo la ungwiro, chilungamo,

10 Pakuti nzeru idzalowa mu mtima mwako,

11 Kuganizira bwino za mʼtsogolo kudzakusunga;

12 Nzeru idzakupulumutsa ku mayendedwe oyipa,

13 amene amasiya njira zolungama

14 amene amakondwera pochita zoyipa

15 Amenewa ndi anthu a njira zawo zokhotakhota,

16 Nzeruyo idzakupulumutsanso kwa mkazi wachigololo;

17 amene wasiya mwamuna wa chitsikana wake

18 Pakuti nyumba yake imatsetserekera ku imfa;

19 Opita kwa iye palibe ndi mmodzi yemwe amabwerera

20 Choncho iwe uziyenda mʼnjira za anthu abwino,

21 Pakuti anthu olungama ndiwo ati adzakhale mʼdziko

22 Koma anthu oyipa adzachotsedwa mʼdzikomo,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado