Provérbios 19

NYA

1 Ndi wabwino munthu wosauka amene amayenda mu ungwiro,

2 Si bwino kuti munthu akhale wopanda nzeru;

3 Uchitsiru wa munthu umamubweretsera zovuta,

4 Chuma chimachulukitsa abwenzi;

5 Mboni yonama sidzalephera kulangidwa;

6 Anthu ambiri amafuna munthu wopatsa kuti awakomere mtima,

7 Ngati munthu wosauka abale ake omwe amadana naye,

8 Iye amene amapeza nzeru ndiye kuti amakonda moyo wake.

9 Mboni yonama sidzalephera kulangidwa,

10 Nʼkosayenera kuti chitsiru chizikhala ndi moyo wamanyado,

11 Nzeru zimapangitsa munthu kukhala wosakwiya msanga;

12 Mkwiyo wa mfumu uli ngati kubangula kwa mkango,

13 Mwana wopusa ndiye tsoka la abambo ake

14 Nyumba ndi chuma ndiye cholowa chochokera kwa makolo;

15 Ulesi umagonetsa tulo tofa nato

16 Amene amamvera malangizo amasunga moyo wake,

17 Amene amakomera mtima osauka amachita ngati wakongoletsa Yehova,

18 Langa mwana wako, chiyembekezo chikanalipo;

19 Munthu waukali woopsa ayenera kulandira chilango;

20 Mvera uphungu ndipo landira malangizo;

21 Munthu amakonzekera zambiri mu mtima mwake,

22 Chimene munthu amafuna ndi chikondi chosatha;

23 Kuopa Yehova kumabweretsa moyo;

24 Munthu waulesi amapisa dzanja lake mʼmbale;

25 Menya munthu wonyoza, ndipo anthu opanda nzeru adzachenjererapo;

26 Mwana wochita ndewu ndi abambo ake ndi kuthamangitsa amayi ake,

27 Mwana wanga, ukaleka kumvera malangizo,

28 Mboni yopanda pake imanyoza cholungama,

29 Chilango chakonzedwa kale kuti chigwere anthu oyipa,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado