1 Ndi wabwino munthu wosauka amene amayenda mu ungwiro,
2 Si bwino kuti munthu akhale wopanda nzeru;
3 Uchitsiru wa munthu umamubweretsera zovuta,
4 Chuma chimachulukitsa abwenzi;
5 Mboni yonama sidzalephera kulangidwa;
6 Anthu ambiri amafuna munthu wopatsa kuti awakomere mtima,
7 Ngati munthu wosauka abale ake omwe amadana naye,
8 Iye amene amapeza nzeru ndiye kuti amakonda moyo wake.
9 Mboni yonama sidzalephera kulangidwa,
10 Nʼkosayenera kuti chitsiru chizikhala ndi moyo wamanyado,
11 Nzeru zimapangitsa munthu kukhala wosakwiya msanga;
12 Mkwiyo wa mfumu uli ngati kubangula kwa mkango,
13 Mwana wopusa ndiye tsoka la abambo ake
14 Nyumba ndi chuma ndiye cholowa chochokera kwa makolo;
15 Ulesi umagonetsa tulo tofa nato
16 Amene amamvera malangizo amasunga moyo wake,
17 Amene amakomera mtima osauka amachita ngati wakongoletsa Yehova,
18 Langa mwana wako, chiyembekezo chikanalipo;
19 Munthu waukali woopsa ayenera kulandira chilango;
20 Mvera uphungu ndipo landira malangizo;
21 Munthu amakonzekera zambiri mu mtima mwake,
22 Chimene munthu amafuna ndi chikondi chosatha;
23 Kuopa Yehova kumabweretsa moyo;
24 Munthu waulesi amapisa dzanja lake mʼmbale;
25 Menya munthu wonyoza, ndipo anthu opanda nzeru adzachenjererapo;
26 Mwana wochita ndewu ndi abambo ake ndi kuthamangitsa amayi ake,
27 Mwana wanga, ukaleka kumvera malangizo,
28 Mboni yopanda pake imanyoza cholungama,
29 Chilango chakonzedwa kale kuti chigwere anthu oyipa,