1 Kuyankha kofatsa kumathetsa mkwiyo,
2 Munthu wanzeru amayankhula zinthu za nzeru,
3 Maso a Yehova ali ponseponse,
4 Kuyankhula kodekha kuli ngati mtengo wopatsa moyo,
5 Chitsiru chimanyoza mwambo wa abambo ake,
6 Munthu wolungama amakhala ndi chuma chambiri,
7 Pakamwa pa anthu anzeru pamafalitsa nzeru;
8 Nsembe za anthu oyipa zimamunyansa Yehova,
9 Ntchito za anthu oyipa zimamunyansa Yehova
10 Amene amasiya njira yabwino adzalangidwa koopsa.
11 Manda ndi chiwonongeko ndi zosabisika pamaso pa Yehova,
12 Wonyoza sakonda kudzudzulidwa;
13 Mtima wokondwa umachititsa nkhope kukhala yachimwemwe,
14 Mtima wa munthu wozindikira zinthu umafunafuna nzeru,
15 Munthu woponderezedwa masiku ake onse amakhala oyipa,
16 Kuli bwino kukhala ndi zinthu pangʼono nʼkumaopa Yehova,
17 Kuli bwino kudyera ndiwo zamasamba pamene pali chikondi,
18 Munthu wopsa mtima msanga amayambitsa mikangano,
19 Njira ya munthu waulesi ndi yowirira ndi mtengo waminga,
20 Mwana wanzeru amakondweretsa abambo ake,
21 Uchitsiru umakondweretsa munthu wopanda nzeru,
22 Popanda uphungu zolinga zako munthu zimalephereka,
23 Munthu amakondwera ndi kuyankha koyenera,
24 Munthu wanzeru amatsata njira yopita ku moyo
25 Yehova amapasula nyumba ya munthu wonyada
26 Maganizo a anthu oyipa amamunyansa Yehova,
27 Munthu wofuna phindu mwachinyengo amavutitsa banja lake,
28 Munthu wolungama amaganizira za mmene ayankhire,
29 Yehova amakhala kutali ndi anthu oyipa,
30 Kuwala kwa maso kumasangalatsa mtima
31 Womvera mawu a chidzudzulo amene apatsa moyo
32 Amene amanyoza mwambo amadzinyoza yekha,
33 Kuopa Yehova kumaphunzitsa munthu nzeru,