Provérbios 14

NYA

1 Mkazi wanzeru amamanga banja lake,

2 Amene amayenda molungama amaopa Yehova,

3 Kuyankhula kwa chitsiru kumamuyitanira ndodo pa msana,

4 Pakasowa ngʼombe zolima gome limakhala lopanda chakudya,

5 Mboni yokhulupirika sinama,

6 Wonyoza anzake amafunafuna nzeru koma osayipeza,

7 Khala kutali ndi munthu wopusa

8 Nzeru za munthu wochenjera zagona pakuzindikira njira zake.

9 Zitsiru zimanyoza za kulapa machimo, awo,

10 Mtima uliwonse umadziwa wokha zowawa zake,

11 Nyumba ya munthu woyipa idzapasuka,

12 Pali njira ina yooneka ngati yabwino kwa munthu,

13 Ngakhale poseka mtima utha kumva kuwawa,

14 Munthu wosakhulupirika adzalandira zogwirizana ndi ntchito yake,

15 Munthu wopusa amakhulupirira chilichonse,

16 Munthu wanzeru amaopa Mulungu ndipo amapewa zoyipa,

17 Munthu wopsa mtima msanga amachita zinthu za uchitsiru,

18 Anthu opusa amalandira uchitsiru,

19 Anthu oyipa adzagwada pamaso pa anthu abwino,

20 Munthu wosauka ngakhale anansi ake omwe amamuda,

21 Wonyoza mnansi wake ndi wochimwa

22 Kodi amene amakonzekera zoyipa sasochera?

23 Ntchito iliyonse imakhala ndi phindu,

24 Chipewa chaulemu cha anthu a nzeru ndi chuma chawo chomwe,

25 Mboni yokhulupirika imapulumutsa miyoyo,

26 Amene amaopa Yehova ali ndi chitetezo chokwanira

27 Kuopa Yehova ndiye kasupe wamoyo,

28 Gulu lalikulu la anthu ndiye ulemerero wa mfumu,

29 Munthu wosapsa mtima msanga amamvetsa zinthu kwambiri,

30 Mtima wodekha umapatsa thupi moyo,

31 Amene amapondereza mʼmphawi amanyoza mlengi wake,

32 Anthu oyipa adzakanthidwa chifukwa cha ntchito zawo zomwe,

33 Nzeru zimakhala mu mtima mwa anthu omvetsa zinthu,

34 Chilungamo chimakweza mtundu wa anthu,

35 Mfumu imasangalatsidwa ndi wantchito wanzeru,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado