Provérbios 12

NYA

1 Munthu amene amakonda mwambo amakonda kudziwa zinthu,

2 Munthu wabwino amapeza kuyanja pamaso pa Yehova,

3 Munthu sangakhazikike bwino pochita zoyipa,

4 Mkazi wakhalidwe labwino ali ngati chipewa chaufumu kwa mwamuna wake,

5 Maganizo a anthu olungama ndi owongoka,

6 Mawu a anthu oyipa ndi ophetsa,

7 Anthu oyipa amagonjetsedwa ndipo amayiwalika,

8 Munthu amatamandidwa malinga ndi nzeru zake,

9 Nʼkwabwino kukhala munthu wonyozeka koma wodzigwirira ntchito nʼkukhala ndi zonse zofunika,

10 Munthu wolungama amasamalira moyo wa ziweto zake,

11 Wolima mʼmunda mwake mwakhama adzakhala ndi chakudya chochuluka,

12 Munthu woyipa amalakalaka zofunkha za anthu oyipa,

13 Munthu woyipa amakodwa mu msampha wa mayankhulidwe ake oyipa;

14 Munthu amakhala ndi zabwino zambiri chifukwa cha mawu ake

15 Zochita za chitsiru mwini wakeyo amaziona ngati zabwino,

16 Mkwiyo wa chitsiru umadziwika nthawi yomweyo,

17 Woyankhula zoona amapereka umboni woona,

18 Munthu woyankhula mosasamala mawu ake amalasa ngati lupanga,

19 Mawu woona amakhala mpaka muyaya

20 Mʼmitima ya anthu amene amakonza zoyipa muli chinyengo;

21 Palibe choyipa chimene chimagwera munthu wolungama,

22 Pakamwa pa bodza pamamunyansa Yehova,

23 Munthu wochenjera amabisa nzeru zake,

24 Ogwira ntchito mwakhama adzalamulira,

25 Nkhawa imakhala ngati katundu wolemera mu mtima mwa munthu,

26 Munthu wolungama amatsogolera mnansi wake,

27 Munthu waulesi sapeza chimene akufuna,

28 Mʼnjira yachilungamo muli moyo;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado