1 Iwe Israeli, usakondwere;
2 Malo opunthira tirigu ndi malo opsinyira mphesa sadzadyetsa anthu;
3 Sadzakhalanso mʼdziko la Yehova.
4 Iwo sadzaperekanso chopereka cha chakumwa kwa Yehova,
5 Kodi mudzachita chiyani pa tsiku la maphwando anu oyikika;
6 Ngakhale iwo atathawa chiwonongeko,
7 Masiku achilango akubwera,
8 Mneneri pamodzi ndi Mulungu wanga
9 Iwo azama mu zachinyengo
10 “Pamene ndinamupeza Israeli
11 Ulemerero wa Efereimu udzawuluka ngati mbalame.
12 Ngakhale atalera ana
13 Ndaona Efereimu ngati Turo,
14 Inu Yehova, muwapatse.
15 “Chifukwa cha zoyipa zawo zonse ku Giligala,
16 Efereimu wathedwa,
17 Mulungu wanga adzawakana