1 Israeli anali mpesa wotambalala;
2 Mtima wawo ndi wonyenga
3 Pamenepo anthuwo adzanena kuti, “Ife tilibe mfumu
4 Mafumu amalonjeza zambiri,
5 Anthu amene amakhala mu Samariya akuchita mantha
6 Fanolo lidzatengedwa kupita ku Asiriya
7 Samariya ndi mfumu yake adzatengedwa kupita kutali
8 Malo opembedzerako mafano a ku Aveni adzawonongedwa.
9 “Iwe Israeli, wachimwa kuyambira mʼmasiku a Gibeya,
10 Pamene ndifunire, ndidzalanga anthuwo;
11 Efereimu ndi mwana wangʼombe wamkazi wophunzitsidwa
12 Mufese nokha chilungamo
13 Koma inu munadzala zolakwa,
14 phokoso lankhondo lidzamveka pakati pa anthu anga
15 Momwemonso zidzakuchitikira, iwe Beteli