1 “Israeli ali mwana, ndinamukonda,
2 Koma ndimati ndikamapitiriza kuyitana
3 Ndi Ine amene ndinaphunzitsa Efereimu kuyenda,
4 Ndinawatsogolera ndi zingwe zachifundo cha anthu
5 “Sadzabwerera ku Igupto,
6 Malupanga adzangʼanima mʼmizinda yawo,
7 Anthu anga atsimikiza zondifulatira Ine.
8 “Kodi ndingakusiye bwanji iwe Efereimu?
9 Sindidzalola kuti ndikulange ndi mkwiyo wanga woopsa,
10 Iwo adzatsatira Yehova;
11 Adzabwera akunjenjemera
12 Efereimu wandizungulira ndi mabodza,