Oséias 8

NYA

1 “Ika lipenga pakamwa pako.

2 Israeli akulirira kwa Ine kuti,

3 Koma Israeli wakana zabwino;

4 Amalonga mafumu mosatsata kufuna kwanga.

5 Iwe Samariya, taya fano lako la mwana wangʼombe!

6 Mafanowa ndi ochokera ku Israeli!

7 “Aisraeli amadzala mphepo

8 Israeli wamezedwa,

9 Pakuti iwo anapita ku Asiriya

10 Ngakhale wadzigulitsa pakati pa mitundu ya anthu,

11 “Ngakhale Efereimu anamanga maguwa ambiri a nsembe zoperekedwa chifukwa cha tchimo,

12 Ndinawalembera zinthu zambiri za malamulo anga,

13 Amapereka nsembe za nyama kwa Ine

14 Israeli wayiwala Mlengi wake

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado