1 “Ika lipenga pakamwa pako.
2 Israeli akulirira kwa Ine kuti,
3 Koma Israeli wakana zabwino;
4 Amalonga mafumu mosatsata kufuna kwanga.
5 Iwe Samariya, taya fano lako la mwana wangʼombe!
6 Mafanowa ndi ochokera ku Israeli!
7 “Aisraeli amadzala mphepo
8 Israeli wamezedwa,
9 Pakuti iwo anapita ku Asiriya
10 Ngakhale wadzigulitsa pakati pa mitundu ya anthu,
11 “Ngakhale Efereimu anamanga maguwa ambiri a nsembe zoperekedwa chifukwa cha tchimo,
12 Ndinawalembera zinthu zambiri za malamulo anga,
13 Amapereka nsembe za nyama kwa Ine
14 Israeli wayiwala Mlengi wake