Oséias 7

NYA

1 Pamene ndichiritsa Israeli,

2 Koma sazindikira kuti Ine

3 “Anthuwa amasangalatsa mfumu ndi zoyipa zawozo,

4 Onsewa ndi anthu azigololo,

5 Pa tsiku la chikondwerero cha mfumu yathu

6 Mitima yawo ili ngati uvuni;

7 Onsewa ndi otentha ngati uvuni,

8 “Efereimu wasakanikirana ndi mitundu ya anthu ena;

9 Alendo atha mphamvu zake,

10 Kunyada kwake Israeli kukumutsutsa,

11 “Efereimu ali ngati nkhunda

12 Akamadzapita, ndidzawakola ndi ukonde wanga;

13 Tsoka kwa iwo,

14 Iwo salirira kwa Ine kuchokera pansi pa mtima,

15 Ine ndinawaphunzitsa ndikuwalimbitsa,

16 Iwo satembenukira kwa Wammwambamwamba;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado