1 Pamene ndichiritsa Israeli,
2 Koma sazindikira kuti Ine
3 “Anthuwa amasangalatsa mfumu ndi zoyipa zawozo,
4 Onsewa ndi anthu azigololo,
5 Pa tsiku la chikondwerero cha mfumu yathu
6 Mitima yawo ili ngati uvuni;
7 Onsewa ndi otentha ngati uvuni,
8 “Efereimu wasakanikirana ndi mitundu ya anthu ena;
9 Alendo atha mphamvu zake,
10 Kunyada kwake Israeli kukumutsutsa,
11 “Efereimu ali ngati nkhunda
12 Akamadzapita, ndidzawakola ndi ukonde wanga;
13 Tsoka kwa iwo,
14 Iwo salirira kwa Ine kuchokera pansi pa mtima,
15 Ine ndinawaphunzitsa ndikuwalimbitsa,
16 Iwo satembenukira kwa Wammwambamwamba;