1 “Bwerani, tiyeni tibwerere kwa Yehova.
2 Pakapita masiku awiri adzatitsitsimutsa;
3 Tiyeni timudziwe Yehova,
4 Iwe Efereimu, kodi ndichite nawe chiyani?
5 Choncho ndakuwazani ngati nkhuni kudzera mwa aneneri anga,
6 Pakuti Ine ndimafuna chifundo osati nsembe,
7 Monga Adamu, anthuwa aphwanya pangano langa,
8 Giliyadi ndi mzinda wa anthu ochita zoyipa,
9 Monga momwe mbala zimadikirira anthu,
10 Ndaona chinthu choopsa kwambiri
11 “Kunenanso za iwe Yuda,