1 “Ansembe inu, imvani izi!
2 Owukira azama mʼmoyo wakupha,
3 Ndimadziwa zonse za Efereimu;
4 “Ntchito zawo siziwalola
5 Kudzikuza kwa Israeli kwakhala umboni womutsutsa;
6 Pamene adzapita ndi nkhosa zawo ndi ngʼombe zawo
7 Iwo ndi osakhulupirika kwa Yehova;
8 “Womba lipenga mu Gibeya,
9 Efereimu adzasanduka bwinja
10 Atsogoleri a Yuda ali ngati anthu
11 Efereimu waponderezedwa,
12 Ine ndili ngati njenjete kwa Efereimu,
13 “Efereimu ataona nthenda yake,
14 Pakuti Ine ndidzakhala ngati mkango kwa Efereimu.
15 Ndipo ndidzabwerera ku malo anga