Oséias 4

NYA

1 Inu Aisraeli, imvani mawu a Yehova,

2 Muli kutemberera kokha, kunama ndi kupha.

3 Chifukwa chake dziko likulira

4 “Koma wina asapeze mnzake chifukwa,

5 Mumapunthwa usana ndi usiku

6 Anthu anga akuwonongeka chifukwa chosadziwa.

7 Ansembe ankati akachuluka

8 Amalemererapo pa machimo a anthu anga

9 Ndipo zidzakhala motere: zochitikira anthu ena, zidzachitikiranso ansembe.

10 “Iwo azidzadya koma sadzakhuta;

11 ku zachiwerewere,

12 za anthu anga.

13 Amapereka nsembe pamwamba pa mapiri

14 “Ine sindidzalanga ana anu aakazi

15 “Ngakhale umachita chigololo, iwe Israeli,

16 Aisraeli ndi nkhutukumve,

17 Efereimu waphathana ndi mafano;

18 Ngakhale pamene zakumwa zawo zatha,

19 Adzachotsedwa ndi kamvuluvulu

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado