1 Inu Aisraeli, imvani mawu a Yehova,
2 Muli kutemberera kokha, kunama ndi kupha.
3 Chifukwa chake dziko likulira
4 “Koma wina asapeze mnzake chifukwa,
5 Mumapunthwa usana ndi usiku
6 Anthu anga akuwonongeka chifukwa chosadziwa.
7 Ansembe ankati akachuluka
8 Amalemererapo pa machimo a anthu anga
9 Ndipo zidzakhala motere: zochitikira anthu ena, zidzachitikiranso ansembe.
10 “Iwo azidzadya koma sadzakhuta;
11 ku zachiwerewere,
12 za anthu anga.
13 Amapereka nsembe pamwamba pa mapiri
14 “Ine sindidzalanga ana anu aakazi
15 “Ngakhale umachita chigololo, iwe Israeli,
16 Aisraeli ndi nkhutukumve,
17 Efereimu waphathana ndi mafano;
18 Ngakhale pamene zakumwa zawo zatha,
19 Adzachotsedwa ndi kamvuluvulu