1 Iwe Israeli bwerera kwa Yehova Mulungu wako.
2 Bweretsani zopempha zanu
3 Asiriya sangatipulumutse;
4 Ine ndidzachiza kusakhulupirika kwawo
5 Ndidzakhala ngati mame kwa Israeli
6 mphukira zake zidzakula.
7 Anthu adzakhalanso mu mthunzi wake.
8 Efereimu adzati, “Ndidzachita nawonso chiyani mafano?
9 Ndani ali ndi nzeru? Adzazindikire zinthu izi.