Oséias 14

NYA

1 Iwe Israeli bwerera kwa Yehova Mulungu wako.

2 Bweretsani zopempha zanu

3 Asiriya sangatipulumutse;

4 Ine ndidzachiza kusakhulupirika kwawo

5 Ndidzakhala ngati mame kwa Israeli

6 mphukira zake zidzakula.

7 Anthu adzakhalanso mu mthunzi wake.

8 Efereimu adzati, “Ndidzachita nawonso chiyani mafano?

9 Ndani ali ndi nzeru? Adzazindikire zinthu izi.

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado